Mlaliki 5:11 - Buku Lopatulika11 Pochuluka katundu, akudyapo achulukanso; nanga apindulira eni ake chiyani, koma kungopenyera ndi maso ao? Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201411 Pochuluka katundu, akudyapo achulukanso; nanga apindulira eni ake chiyani, koma kungopenyera ndi maso ao? Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa11 Chuma chikachuluka, odya nawo chumacho amachulukanso. Nanga mwini wake amapindulapo chiyani? Si kumangoziyang'ana basi? Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero11 Chuma chikachuluka akudya nawo chumacho amachulukanso. Nanga mwini wake amapindulapo chiyani kuposa kumangochiyangʼana ndi maso ake? Onani mutuwo |