Mlaliki 5:13 - Buku Lopatulika13 Pali choipa chovuta ndachiona kunja kuno, ndicho, chuma chilikupweteka eni ake pochikundika; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201413 Pali choipa chovuta ndachiona kunja kuno, ndicho, chuma chilikupweteka eni ake pochikundika; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa13 Pansi pano pali choipa china chomvetsa chisoni kwambiri chimene ndachiwona: Chuma chopweteka mwiniwake yemwe. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero13 Ine ndinaona choyipa chomvetsa chisoni pansi pano: chuma chokundikidwa chikupweteka mwini wake yemwe, Onani mutuwo |