Mlaliki 4:5 - Buku Lopatulika5 Chitsiru chimanga manja ake, ndipo chidya nyama yakeyake. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20145 Chitsiru chimanga manja ake, nichidya nyama yakeyake. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa5 Paja akuti chitsiru chimangoti manja khodobala, nkumasoŵa chakudya mpaka kumafa ndi njala. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero5 Chitsiru chimangoti manja ake lobodo ndi kudzipha chokha ndi njala. Onani mutuwo |