Mlaliki 4:3 - Buku Lopatulika3 inde yemwe sanabadwe konse aposa onse awiriwo popeza sanaone ntchito yoipa yochitidwa kunja kuno. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20143 inde yemwe sanabadwe konse aposa onse awiriwo popeza sanaone ntchito yoipa yochitidwa kunja kuno. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa3 Koma wopambana onsewo ndi amene sadabadwe nkomwe, ndipo ntchito zoipa zimene zimachitika pansi pano sadaziwone. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero3 Koma wopambana onsewa ndi amene sanabadwe, amene sanaone zoyipa zimene chimachitika pansi pano. Onani mutuwo |