Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Mlaliki 4:2 - Buku Lopatulika

2 Ndipo ndinatama akufa atatha kufa kupambana amoyo omwe alipobe;

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

2 Ndipo ndinatama akufa atatha kufa kupambana amoyo omwe alipobe;

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

2 Ndinkaganiza kuti akufa aja amene adapita kale ndi amwai kwambiri kupambana amene akadali ndi moyo.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

2 Ndipo ndinanena kuti akufa, amene anafa kale, ndi osangalala kuposa amoyo, amene akanalibe ndi moyo.

Onani mutuwo Koperani




Mlaliki 4:2
5 Mawu Ofanana  

Chifukwa chake ndinada moyo; pakuti ntchito azipanga kunja kuno zindisautsa; pakuti zonse ndi chabe ndi kungosautsa mtima.


Mbiri yabwino iposa zonunkhira zabwino; ndi tsiku lakumwalira liposa tsiku lakubadwa.


Musamlirire wakufa, musachite maliro ake; koma mumliritse iye amene amuka, pakuti sadzabweranso, kapena kuonanso dziko la kwao.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa