Mlaliki 4:13 - Buku Lopatulika13 Mnyamata wosauka ndi wanzeru apambana mfumu yokalamba ndi yopusa, imene sifunanso kulangidwa mwambo. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201413 Mnyamata wosauka ndi wanzeru apambana mfumu yokalamba ndi yopusa, imene sifunanso kulangidwa mwambo. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa13 Mnyamata wosauka ndi wanzeru ali bwino kupambana mfumu yokalamba ndi yopusa, imene siikumvanso malangizo. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero13 Wachinyamata wosauka koma wanzeru aposa mfumu yokalamba koma yopusa imene simvanso malangizo. Onani mutuwo |