Mlaliki 4:12 - Buku Lopatulika12 Ndipo wina akamgonjetsa mmodziyo, awiri adzachilimika; ndipo chingwe cha nkhosi zitatu sichiduka msanga. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201412 Ndipo wina akamlaka mmodziyo, awiri adzachilimika; ndipo chingwe cha m'khosi zitatu sichiduka msanga. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa12 Nkotheka kuti munthu apambane mnzake amene ali yekha, koma pakakhala aŵiri, iwoŵa adzalimbana naye. Chingwe cha nkhosi zitatu sichidukirapo. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero12 Munthu mmodzi angathe kugonjetsedwa, koma anthu awiri akhoza kudziteteza. Chingwe cha maulusi atatu sichidukirapo. Onani mutuwo |