Mlaliki 4:11 - Buku Lopatulika11 Ndiponso awiri akagona limodzi afunditsana; koma mmodzi pa yekha kodi adzafunditsidwa bwanji? Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201411 Ndiponso awiri akagona limodzi afunditsana; koma mmodzi pa yekha kodi adzafunditsidwa bwanji? Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa11 Ndiponso aŵiri akagona pamodzi amafunditsana. Koma nanga mmodzi angathe kudzifunditsa bwanji? Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero11 Komanso ngati anthu awiri agona malo amodzi, adzafunditsana. Koma nanga mmodzi angadzifunditse yekha? Onani mutuwo |