Mlaliki 4:14 - Buku Lopatulika14 Pakuti atuluka m'nyumba yandende kulowa ufumu; komanso yemwe abadwa m'dziko lake asauka. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201414 Pakuti atuluka m'nyumba yandende kulowa ufumu; komanso yemwe abadwa m'dziko lake asauka. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa14 Mnyamatayo atha kukhala kuti adachita kuchokera ku ndende kudzaloŵa ufumu, kapenanso kuti adabadwa mmphaŵi m'dziko mwake momwemo. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero14 Wachinyamatayo angathe kuchokera ku ndende ndi kudzakhala mfumu, kapena angathe kubadwa wosauka mʼdziko la mfumuyo. Onani mutuwo |