Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Mlaliki 3:9 - Buku Lopatulika

9 Wogwira Ntchito aona phindu lanji m'chomsautsacho?

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

9 Wogwira Ntchito aona phindu lanji m'chomsautsacho?

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

9 Kodi wantchito amapeza phindu lanji pa ntchito yake yolemetsa?

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

9 Kodi wantchito amapeza phindu lanji pa ntchito yake yolemetsa?

Onani mutuwo Koperani




Mlaliki 3:9
7 Mawu Ofanana  

M'ntchito zonse muli phindu; koma kulankhulalankhula kungopatsa umphawi.


Kodi ntchito zake zonse munthu asauka nazo zimpindulira chiyani?


Pamenepo ndinayang'ana zonse manja anga anazipanga, ndi ntchito zonse ndinasauka pozigwira; ndipo taona, zonse zinali zachabechabe ndi kungosautsa mtima, ndipo kunalibe phindu kunja kuno.


Ichinso ndi choipa chowawa, chakuti adzangopita monse monga anadza; ndipo wodzisautsa chabe adzaona phindu lanji?


Pakuti munthu adzapindulanji, akalandira dziko lonse, nataya moyo wake? Kapena munthu adzaperekanji chosintha ndi moyo wake?


kuti inunso muvomere otere, ndi yense wakuchita nao, ndi kugwiritsa ntchito.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa