Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Mlaliki 3:10 - Buku Lopatulika

10 Ndaona vuto limene Mulungu wapatsa ana a anthu kuti avutidwe nalo.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

10 Ndaona vuto limene Mulungu wapatsa ana a anthu kuti avutidwe nalo.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

10 Ndaziwona ntchito zimene Mulungu adapatsa anthu kuti azizigwira.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

10 Ine ndinaona chipsinjo chimene Mulungu anayika pa anthu.

Onani mutuwo Koperani




Mlaliki 3:10
6 Mawu Ofanana  

m'thukuta la nkhope yako udzadya chakudya, kufikira kuti udzabwerera kunthaka: chifukwa kuti m'menemo unatengedwa: chifukwa kuti ndiwe fumbi, ndi kufumbiko udzabwerera.


Monga sudziwa njira ya mphepo, ngakhale makulidwe a mafupa m'mimba ya mkazi ali ndi pakati; momwemo sudziwa ntchito za Mulungu amene achita zonse.


Pakuti yemwe Mulungu amuyesa wabwino ampatsa nzeru ndi chidziwitso ndi chimwemwe; koma wochimwa amlawitsa vuto la kusonkhanitsa ndi kukundika, kuti aperekere yemwe Mulungu amuyesa wabwino. Ichinso ndi chabe ndi kungosautsa mtima.


Pakuti mukumbukira, abale, chigwiritso chathu ndi chivuto chathu; pochita usiku ndi usana, kuti tingalemetse wina wa inu, tinalalikira kwa inu Uthenga Wabwino wa Mulungu.


kapena sitinadye mkate chabe padzanja la munthu aliyense, komatu m'chivuto ndi chipsinjo, tinagwira ntchito usiku ndi usana, kuti tingalemetse wina wa inu;


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa