Mlaliki 3:10 - Buku Lopatulika10 Ndaona vuto limene Mulungu wapatsa ana a anthu kuti avutidwe nalo. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201410 Ndaona vuto limene Mulungu wapatsa ana a anthu kuti avutidwe nalo. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa10 Ndaziwona ntchito zimene Mulungu adapatsa anthu kuti azizigwira. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero10 Ine ndinaona chipsinjo chimene Mulungu anayika pa anthu. Onani mutuwo |