Mlaliki 3:8 - Buku Lopatulika8 mphindi yakukonda ndi mphindi yakudana; mphindi ya nkhondo ndi mphindi ya mtendere. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20148 mphindi yakukonda ndi mphindi yakudana; mphindi ya nkhondo ndi mphindi ya mtendere. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa8 Pali nthaŵi yokondana ndi nthaŵi yodana, nthaŵi ya nkhondo ndi nthaŵi ya mtendere. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero8 Nthawi yokondana ndi nthawi yodana, nthawi ya nkhondo ndi nthawi ya mtendere. Onani mutuwo |