Mlaliki 3:7 - Buku Lopatulika7 mphindi yakung'amba ndi mphindi yakusoka; mphindi yakutonthola ndi mphindi yakulankhula; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20147 mphindi yakung'amba ndi mphindi yakusoka; mphindi yakutonthola ndi mphindi yakulankhula; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa7 Pali nthaŵi yong'amba ndi nthaŵi yosoka, nthaŵi yokhala chete ndi nthaŵi yolankhula. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero7 Nthawi yongʼamba ndi nthawi yosoka, nthawi yokhala chete ndi nthawi yoyankhula. Onani mutuwo |