Mlaliki 3:6 - Buku Lopatulika6 mphindi yakufunafuna ndi mphindi yakumwazika; mphindi yakusunga ndi mphindi yakutaya; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20146 mphindi yakufunafuna ndi mphindi yakumwazika; mphindi yakusunga ndi mphindi yakutaya; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa6 Pali nthaŵi yofunafuna ndi nthaŵi yotaya, nthaŵi yosunga ndi nthaŵi yomwaza. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero6 Nthawi yofunafuna ndi nthawi yoleka kufunafuna, nthawi yosunga ndi nthawi yotaya. Onani mutuwo |