Mlaliki 3:5 - Buku Lopatulika5 mphindi yakutaya miyala ndi mphindi yakukundika miyala; mphindi yakufungatirana ndi mphindi yakuleka kufungatirana; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20145 mphindi yakutaya miyala ndi mphindi yakukundika miyala; mphindi yakufungatirana ndi mphindi yakuleka kufungatirana; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa5 Pali nthaŵi yokhala malo amodzi ndi nthaŵi yotalikirana, nthaŵi yokumbatirana ndi nthaŵi yoleka zokumbatiranazo. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero5 Nthawi yotaya miyala ndi nthawi yokundika miyala, nthawi yokumbatirana ndi nthawi yoleka kukumbatirana. Onani mutuwo |