Mlaliki 3:4 - Buku Lopatulika4 mphindi yakugwa misozi ndi mphindi yakuseka; mphindi yakulira ndi mphindi yakuvina; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20144 mphindi yakugwa misozi ndi mphindi yakuseka; mphindi yakulira ndi mphindi yakuvina; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa4 Pali nthaŵi yomva chisoni ndi nthaŵi yosangalala, nthaŵi yolira maliro ndi nthaŵi yovina. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero4 Nthawi yomva chisoni ndi nthawi yosangalala, nthawi yolira maliro ndi nthawi yovina. Onani mutuwo |