Mlaliki 3:3 - Buku Lopatulika3 mphindi yakupha ndi mphindi yakuchiza; mphindi yakupasula ndi mphindi yakumanga; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20143 mphindi yakupha ndi mphindi yakuchiza; mphindi yakupasula ndi mphindi yakumanga; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa3 Pali nthaŵi yakupha ndi nthaŵi yochiritsa, nthaŵi yogwetsa ndi nthaŵi yomanga. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero3 Nthawi yakupha ndi nthawi yochiritsa, nthawi yogwetsa ndi nthawi yomanga. Onani mutuwo |