Mlaliki 2:5 - Buku Lopatulika5 ndinakonza mphanje ndi minda yanga, ndi kuokamo mitengo ya zipatso za mitundumitundu; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20145 ndinakonza mphanje ndi minda yanga, ndi kuokamo mitengo ya zipatso za mitundumitundu; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa5 Ndidaalima madimba ndi minda ya mitengo. Ndidaabzalamo mitengo yazipatso ya mitundu yonse. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero5 Ndinalima madimba ndi minda yamitengo; ndipo ndinadzalamo mitengo ya zipatso za mitundu yonse. Onani mutuwo |