Mlaliki 2:4 - Buku Lopatulika4 Ndinadzipangira zazikulu; ndinadzimangira nyumba; ndi kuoka mipesa; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20144 Ndinadzipangira zazikulu; ndinadzimangira nyumba; ndi kuoka mipesa; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa4 Ndidaachita ntchito zazikulu. Ndidaamanga nyumba zambiri, ndi kudziwokera mipesa. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero4 Ndinagwira ntchito zikuluzikulu: Ndinadzimangira nyumba ndi kuwoka mipesa. Onani mutuwo |