Mlaliki 2:6 - Buku Lopatulika6 ndinadzipangira ndekha matamanda a madzi akuthirira madzi m'nkhalango momeramo mitengo; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20146 ndinadzipangira ndekha matamanda a madzi akuthirira madzi m'nkhalango momeramo mitengo; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa6 Ndidaakumbanso maiŵe oti madzi ake azithirira minda ya mitengo yobzala ija. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero6 Ndinakumba mayiwe osungiramo madzi woti ndizithirira minda ya mitengo yodzalidwa ija. Onani mutuwo |