Mlaliki 2:18 - Buku Lopatulika18 Ndipo ndinada ntchito zanga zonse ndinasauka nazo kunja kuno; pakuti ndidzamsiyira izo munthu wina amene adzanditsata. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201418 Ndipo ndinada ntchito zanga zonse ndinasauka nazo kunja kuno; pakuti ndidzamsiyira izo munthu wina amene adzanditsata. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa18 Ntchito zanga zonse zolemetsa zimene ndidazigwira pansi pano zidandiipira, chifukwa ndiyenera kuzisiyira amene adzabwere pambuyo panga. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero18 Ine ndinadana nazo ntchito zonse zimene ndinazigwira pansi pano, chifukwa ndinayenera kudzazisiyira wina amene adzalowa mʼmalo mwanga. Onani mutuwo |