Mlaliki 2:10 - Buku Lopatulika10 Ndipo chilichonse maso anga anachifuna sindinawamane; sindinakanize mtima wanga chimwemwe chilichonse pakuti mtima wanga unakondwera ndi ntchito zanga zonse; gawo langa la m'ntchito zanga zonse ndi limeneli. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201410 Ndipo chilichonse maso anga anachifuna sindinawamana; sindinakaniza mtima wanga chimwemwe chilichonse pakuti mtima wanga unakondwera ndi ntchito zanga zonse; gawo langa la m'ntchito zanga zonse ndi limeneli. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa10 Chilichonse chimene maso anga ankachilakalaka, ndidaachitenga. Mtima wanga sindidaumane zokondweretsazo, pakuti mtima wangawo unkakondwa ndi ntchito zanga zonse zolemetsa. Zimenezi zinali mphotho ya ntchito zanga zolemetsazo. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero10 Sindinadzimane chilichonse chimene maso anga anachifuna; mtima wanga sindinawumane zokondweretsa. Mtima wanga unakondwera ndi ntchito yanga yonse, ndipo iyi ndiyo inali mphotho ya ntchito zanga zonse zolemetsa. Onani mutuwo |