Mlaliki 12:9 - Buku Lopatulika9 Ndiponso pokhala wanzeru Mlalikiyo anaphunzitsabe anthu nzeru; inde, anatchera makutu nafunafuna nalongosola miyambi yambiri. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20149 Ndiponso pokhala wanzeru Mlalikiyo anaphunzitsabe anthu nzeru; inde, anatchera makutu nafunafuna nalongosola miyambi yambiri. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa9 Chifukwa chakuti Mlalikiyo anali waluntha, adaphunzitsa anthu zambiri. Ankasinkhasinkha, kufufuzafufuza ndi kulongosola malangizo mosamala kwambiri. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero9 Mlaliki sanali wozindikira zinthu kokha ayi, komanso ankaphunzitsa anthu. Iye ankasinkhasinkha ndi kufufuzafufuza ndi kulemba mwadongosolo miyambi yambiri. Onani mutuwo |