Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Mlaliki 12:10 - Buku Lopatulika

10 Mlalikiyo anasanthula akapeze mau okondweretsa, ndi zolemba zoongoka ngakhale mau oona.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

10 Mlalikiyo anasanthula akapeze mau okondweretsa, ndi zolemba zoongoka ngakhale mau oona.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

10 Mlalikiyo ankafunafuna mau ogwira mtima, ndipo adalemba mau oona ndi mtima wolungama.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

10 Mlaliki anafufuzafufuza kuti apeze mawu oyenera, ndipo zimene analemba zinali zolondola ndiponso zoona.

Onani mutuwo Koperani




Mlaliki 12:10
14 Mawu Ofanana  

Milomo ya wolungama idziwa zokondweretsa; koma m'kamwa mwa oipa munena zokhota.


Munthu akondwera ndi mayankhidwe a m'kamwa mwake; ndi mau a pa nthawi yake kodi sali abwino?


Ziwembu zoipa zinyansa Yehova; koma oyera mtima alankhula mau okondweretsa.


Mau a Mlaliki, mwana wa Davide, mfumu ya mu Yerusalemu.


Ine Mlaliki ndinali mfumu ya Israele mu Yerusalemu.


Indetu, indetu, ndinena kwa iwe, Tilankhula chimene tichidziwa, ndipo tichita umboni za chimene tachiona; ndipo umboni wathu simuulandira.


chifukwa cha chiyembekezo chosungikira kwa inu mu Mwamba, chimene mudachimva kale m'mau a choonadi cha Uthenga Wabwino,


Mauwa ali okhulupirika ndi oyenera konse kuti awalandire, kuti Khristu Yesu anadza kudziko lapansi kupulumutsa ochimwa; wa iwowa ine ndine woposa;


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa