Mlaliki 10:2 - Buku Lopatulika2 Wanzeru, mtima wake uli kudzanja lake lamanja; koma chitsiru, mtima wake kulamanzere. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20142 Wanzeru, mtima wake uli kudzanja lake lamanja; koma chitsiru, mtima wake kulamanzere. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa2 Mtima wa munthu wanzeru umamtsogolera bwino, koma mtima wa munthu wopusa umamsokeza. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero2 Mtima wa munthu wanzeru umamutsogolera bwino, koma mtima wa munthu wopusa umamusocheretsa. Onani mutuwo |