Mlaliki 10:16 - Buku Lopatulika16 Tsoka kwa dzikowe, pamene mfumu yako ndiye mwana, ndipo akalonga ako adyera mamawa! Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201416 Tsoka kwa dzikowe, pamene mfumu yako ndiye mwana, ndipo akalonga ako adyera mamawa! Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa16 Tsoka kwa iwe dziko, ngati mfumu yako ikali mwana, ndipo nduna zako zimachezera madyerero usiku wonse. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero16 Tsoka kwa iwe, iwe dziko ngati mfumu yako ikali mwana, ndipo atsogoleri ako amakhala pa madyerero mmamawa. Onani mutuwo |