Mlaliki 10:15 - Buku Lopatulika15 Ntchito ya zitsiru izitopetsa zonsezo, pakuti sichidziwa kunka kumzinda. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201415 Ntchito ya zitsiru izitopetsa zonsezo, pakuti sichidziwa kunka kumudzi. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa15 Chitsiru chimagwira ntchito modzitopetsa, koma njira yopita ku mzinda sichiidziŵa. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero15 Chitsiru chimatopa msanga ndi ntchito yochepa; ndipo sichikhala ndi mphamvu zobwererera ku mudzi. Onani mutuwo |