Mlaliki 10:12 - Buku Lopatulika12 Mau a m'kamwa mwa munthu wanzeru nga chisomo; koma milomo ya chitsiru idzachimeza. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201412 Mau a m'kamwa mwa munthu wanzeru nga chisomo; koma milomo ya chitsiru idzachimeza. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa12 Mau a pakamwa pa munthu wanzeru amakondweretsa, koma pakamwa pa chitsiru mpoononga. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero12 Mawu a pakamwa pa munthu wanzeru ndi okondweretsa, koma chitsiru chidzawonongedwa ndi milomo yake yomwe. Onani mutuwo |