Mlaliki 10:13 - Buku Lopatulika13 Chiyambi cha mau a m'kamwa mwake ndi utsiru; ndipo chimaliziro cha m'kamwa mwake ndi misala yoipa. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201413 Chiyambi cha mau a m'kamwa mwake ndi utsiru; ndipo chimaliziro cha m'kamwa mwake ndi misala yoipa. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa13 Chitsiru chimayamba ndi mau opusa, potsiriza zolankhula zake zimangokhala zamisala basi. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero13 Chitsiru chimayamba ndi mawu opusa; potsiriza pake zoyankhula zake ndi zamisala Onani mutuwo |