Mika 7:8 - Buku Lopatulika8 Usandiseka, mdani wangawe; pakugwa ine ndidzaukanso; pokhala ine mumdima Yehova adzakhala kuunika kwanga. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20148 Usandiseka, mdani wangawe; pakugwa ine ndidzaukanso; pokhala ine mumdima Yehova adzakhala kuunika kwanga. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa8 Inu adani athu musatiseke. Tidagwa inde, koma tidzadzukanso. Ngakhale tikhale mu mdima, Chauta ndiye nyale yathu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero8 Iwe mdani wanga, usandiseke! Ngakhale ndagwa, ndidzauka. Ngakhale ndikukhala mu mdima, Yehova ndiye kuwunika kwanga. Onani mutuwo |