Mika 7:7 - Buku Lopatulika7 Koma ine, ndidzadikira Yehova; ndidzalindirira Mulungu wa chipulumutso changa; Mulungu wanga adzandimvera. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20147 Koma ine, ndidzadikira Yehova; ndidzalindirira Mulungu wa chipulumutso changa; Mulungu wanga adzandimvera. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa7 Koma ine ndidzadalira Chauta. Ndidzaika mtima pa Mulungu Mpulumutsi wanga. Mulungu wanga adzandimva. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero7 Koma ine ndikudikira Yehova mwachiyembekezo, ndikudikira Mulungu Mpulumutsi wanga; Mulungu wanga adzamvetsera. Onani mutuwo |