Mika 7:3 - Buku Lopatulika3 Manja ao onse awiri agwira choipa kuchichita ndi changu; kalonga apempha, ndi woweruza aweruza chifukwa cha mphotho; ndi wamkuluyo angonena chosakaza moyo wake; ndipo achiluka pamodzi. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20143 Manja ao onse awiri agwira choipa kuchichita ndi changu; kalonga apempha, ndi woweruza aweruza chifukwa cha mphotho; ndi wamkuluyo angonena chosakaza moyo wake; ndipo achiluka pamodzi. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa3 Ndi akatswiri pochita zoipa. Akalonga ndi aweruzi amafuna ziphuphu, ndipo mtsogoleri amaŵauza zoipa zimene afuna kuti iwo achite. Motero amalakwira pamodzi. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero3 Manja awo onse ndi aluso pochita zoyipa; wolamulira amafuna mphatso, woweruza amalandira ziphuphu, anthu amphamvu amalamula kuti zichitike zimene akuzifuna, onse amagwirizana zochita. Onani mutuwo |