Mika 7:13 - Buku Lopatulika13 Koma dziko lidzakhala labwinja chifukwa cha iwo okhalamo, mwa zipatso za machitidwe ao. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201413 Koma dziko lidzakhala labwinja chifukwa cha iwo okhalamo, mwa zipatso za machitidwe ao. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa13 Koma dziko lapansi lidzasanduka chipululu chifukwa cha zoipa za anthu ake. Amenewo ndiwo malipiro a ntchito zao. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero13 Dziko lapansi lidzasanduka chipululu chifukwa cha anthu okhala mʼdzikomo, potsatira zochita za anthuwo. Onani mutuwo |