Mika 6:3 - Buku Lopatulika3 Anthu anga inu, ndakuchitirani chiyani? Ndakulemetsani ndi chiyani? Chitani umboni wonditsutsa. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20143 Anthu anga inu, ndakuchitirani chiyani? Ndakulemetsani ndi chiyani? Chitani umboni wonditsutsa. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa3 Chauta akuti, “Inu anthu anga, kodi ndakuchitani chiyani? Kodi ndakutopetsani nchiyani? Tandiyankhani! Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero3 “Anthu anga, kodi ndakuchitirani chiyani? Kodi ndakutopetsani bwanji? Ndiyankheni. Onani mutuwo |