Mika 6:13 - Buku Lopatulika13 Chifukwa chake Inenso ndakukantha ndi kukupweteketsa; ndakupulula chifukwa cha zochimwa zako. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201413 Chifukwa chake Inenso ndakukantha ndi kukupweteketsa; ndakupulula chifukwa cha zochimwa zako. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa13 Nchifukwa chake ndayambapo kukukanthani, kukuwonongani chifukwa cha machimo anu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero13 Choncho, ndayamba kukuwonongani, kukusakazani chifukwa cha machimo anu. Onani mutuwo |