Mika 6:14 - Buku Lopatulika14 Udzadya koma osakhuta; ndi njala yako idzakhala pakati pako; ndipo udzachotsa koma osalanditsa; ndi ichi wachilanditsa ndidzachipereka kulupanga. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201414 Udzadya koma osakhuta; ndi njala yako idzakhala pakati pako; ndipo udzachotsa koma osalanditsa; ndi ichi wachilanditsa ndidzachipereka kulupanga. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa14 Mudzadya, koma simudzakhuta. Njala sidzakuchokani. Mudzakundika zinthu, koma sizidzasungika. Zimene mudzakundika zidzaonongedwa pa nkhondo. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero14 Mudzadya, koma simudzakhuta; mudzakhalabe ndi njala. Mudzasunga zinthu, koma sizidzasungika, chifukwa zimene mudzasunga zidzawonongedwa ndi lupanga. Onani mutuwo |