Mika 6:12 - Buku Lopatulika12 Pakuti anthu ake olemera adzala ndi chiwawa, ndi okhalamo amanena bodza, ndi lilime lao limachita monyenga m'kamwa mwao. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201412 Pakuti anthu ake olemera adzala ndi chiwawa, ndi okhalamo amanena bodza, ndi lilime lao limachita monyenga m'kamwa mwao. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa12 Anthu olemera amachita zankhondo. Anthu onse ndi abodza, amangokhalira kunama. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero12 Anthu ake olemera amachita zachiwawa; anthu ake ndi abodza ndipo pakamwa pawo pamayankhula zachinyengo. Onani mutuwo |