Mika 6:11 - Buku Lopatulika11 Kodi ndikhoza kuyera ndi miyeso yoipa, ndi thumba la miyala yonyenga? Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201411 Kodi ndikhoza kuyera ndi miyeso yoipa, ndi thumba la miyala yonyenga? Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa11 Kodi ndingathe kulekerera munthu amene ali ndi sikelo zobera anzake ndiponso miyeso yonyenga? Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero11 Kodi ndimutenge ngati wosalakwa munthu amene ali ndi sikelo yachinyengo, ndiponso miyeso yabodza mʼthumba lake? Onani mutuwo |