Mika 6:10 - Buku Lopatulika10 Kodi m'nyumba ya woipa mukali chuma chosalungama, ndi muyeso wochepa umene ayenera kuipidwa nao? Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201410 Kodi m'nyumba ya woipa mukali chuma chosalungama, ndi muyeso wochepa umene ayenera kuipidwa nao? Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa10 Kodi Ine ndingathe kuiŵala chuma chimene chili m'nyumba za anthu oipa, chimene adachipata monyenga, ndiponso muyeso wopereŵera umene uli wotembereredwa? Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero10 Inu anthu oyipa, kodi Ine nʼkuyiwala chuma chanu chimene munachipeza mwachinyengo, ndiponso muyeso wanu woperewera umene ndi wotembereredwa? Onani mutuwo |