Mika 6:9 - Buku Lopatulika9 Mau a Yehova aitana mzinda, ndi wanzeru aopa dzina lanu; tamverani ndodo, ndi Iye amene anaiika. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20149 Mau a Yehova aitana mudzi, ndi wanzeru aopa dzina lanu; tamverani ndodo, ndi Iye amene anaiika. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa9 Ndi nzeru kuwopa dzina la Chauta. Akuuza mzinda wa Yerusalemu kuti, “Imvani, inu anthu onse okhala mumzinda muno. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero9 Tamverani! Yehova akuyitana anthu okhala mu mzinda ndi nzeru kuopa dzina lanu. “Mverani mfumu ndi Iye amene anayikhazikitsa. Onani mutuwo |