Mika 5:8 - Buku Lopatulika8 Ndipo otsala a Yakobo adzakhala mwa amitundu, pakati pa mitundu yambiri ya anthu, ngati mkango mwa nyama zakuthengo, ngati msona wa mkango mwa magulu a nkhosa; umenewo ukapitako, upondereza, numwetula, ndipo palibe wakupulumutsa. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20148 Ndipo otsala a Yakobo adzakhala mwa amitundu, pakati pa mitundu yambiri ya anthu, ngati mkango mwa nyama zakuthengo, ngati msona wa mkango mwa magulu a nkhosa; umenewo ukapitako, upondereza, numwetula, ndipo palibe wakupulumutsa. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa8 Onse otsalira a Yakobe adzakhala temberero pakati pa mitundu ya anthu, ngati mkango pakati pa nyama zam'nkhalango. Adzakhala ngati mwana wa mkango, pakati pa gulu la nkhosa, amene amati akadzaziloŵerera, amazimbwandira ndi kuzikadzula. Ndipo sipakhala wozipulumutsa. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero8 Otsala a Yakobo adzakhala pakati pa mitundu ya anthu, mʼgulu la anthu a mitundu yambiri, ngati mkango pakati pa nyama za mʼnkhalango. Ngati mwana wa mkango pakati pa gulu la nkhosa, amene pozidutsa amazidya ndi kuzikhadzula, ndipo palibe angathe kuzilanditsa. Onani mutuwo |