Mika 5:6 - Buku Lopatulika6 Ndipo iwo adzatha dziko la Asiriya ndi lupanga, ndi dziko la Nimirodi, ndilo polowera pake; ndipo adzatilanditsa kwa a ku Asiriya pamene alowa m'dziko lathu, pamene aponda m'kati mwa malire athu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20146 Ndipo iwo adzatha dziko la Asiriya ndi lupanga, ndi dziko la Nimirodi, ndilo polowera pake; ndipo adzatilanditsa kwa a ku Asiriya pamene alowa m'dziko lathu, pamene aponda m'kati mwa malire athu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa6 Iwowo adzagonjetsa dziko la Asiriya ndi lupanga, dziko la Nimirodi adzalilamulira mwankhondo. Adzatipulumutsa kwa Aasiriya, iwowo akadzakaloŵa m'dziko mwathu, kudzatithira nkhondo. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero6 Iwo adzagonjetsa dziko la Asiriya ndi lupanga, dziko la Nimurodi adzalilamulira mwankhondo. Adzatipulumutsa kwa Asiriya akadzafika mʼmalire a mʼdziko lathu kudzatithira nkhondo. Onani mutuwo |