Mika 5:4 - Buku Lopatulika4 Ndipo adzaimirira, nadzadyetsa nkhosa zake mu mphamvu ya Yehova, mu ukulu wa dzina la Yehova Mulungu wake; ndipo iwo adzakhalabe; pakuti pamenepo Iye adzakhala wamkulu kufikira malekezero a dziko lapansi. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20144 Ndipo adzaimirira, nadzadyetsa nkhosa zake mu mphamvu ya Yehova, m'ukulu wa dzina la Yehova Mulungu wake; ndipo iwo adzakhalabe; pakuti pamenepo Iye adzakhala wamkulu kufikira malekezero a dziko lapansi. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa4 Iye adzalimbikira, ndipo adzaŵeta nkhosa zake mwa mphamvu za Chauta ndi ulemerero wa dzina la Chauta, Mulungu wake. Ndipo iwo adzakhala mu mtendere, poti ukulu wake udzakhazikika pa dziko lonse lapansi. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero4 Iye adzalimbika, ndipo adzaweta nkhosa zake mwa mphamvu ya Yehova, mu ulemerero wa dzina la Yehova Mulungu wake. Ndipo iwo adzakhala mu mtendere, pakuti ukulu wake udzakhala ponseponse pa dziko lapansi. Onani mutuwo |