Mika 5:3 - Buku Lopatulika3 Chifukwa chake Iye adzawapereka kufikira nthawi yoti wobalayo wabala; pamenepo otsala a abale ake adzabwera pamodzi ndi ana a Israele. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20143 Chifukwa chake Iye adzawapereka kufikira nthawi yoti wobalayo wabala; pamenepo otsala a abale ake adzabwera pamodzi ndi ana a Israele. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa3 Nchifukwa chake Mulungu adzasiya Israele mpaka pa nthaŵi yoti achire mkazi amene adzabale mwana. Pamenepo, otsala a mtundu wake adzabwereranso kwa Aisraele anzao. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero3 Nʼchifukwa chake Israeli adzasiyidwa mpaka pa nthawi imene mayi amene ali woyembekezera adzachire. Ndipo abale ake onse otsalira adzabwerera kudzakhala pamodzi ndi Aisraeli. Onani mutuwo |