Mika 5:14 - Buku Lopatulika14 Ndipo ndidzazula zifanizo zako m'kati mwako, ndi kutha mizinda yako. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201414 Ndipo ndidzazula zifanizo zako m'kati mwako, ndi kutha midzi yako. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa14 Ndidzagwetsa mafano anu a Asera m'dziko mwanu, ndipo ndidzaononga mizinda yake. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero14 Ndidzazula mitengo ya mafano a Asera imene ili pakati panu, ndipo ndidzawononga mizinda yanu. Onani mutuwo |