Mika 5:13 - Buku Lopatulika13 ndidzaononganso mafano ako osema, ndi zoimiritsa zako pakati pako; ndipo sudzalambiranso ntchito za manja ako. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201413 ndidzaononganso mafano ako osema, ndi zoimiritsa zako pakati pako; ndipo sudzalambiranso ntchito za manja ako. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa13 Ndidzaononga mafano anu onse pamodzi ndi miyala yoimika yopembedzerapo m'dziko mwanu. Simudzazigwadiranso zinthuzo zimene mudapanga ndi manja anu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero13 Ndidzawononga mafano anu osema pamodzi ndi miyala yanu yopatulika imene ili pakati panu; simudzagwadiranso zinthu zopanga ndi manja anu. Onani mutuwo |