Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Mika 5:15 - Buku Lopatulika

15 Ndipo ndidzabwezera amitundu osamvera chilango mu mkwiyo waukali.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

15 Ndipo ndidzabwezera amitundu osamvera chilango mu mkwiyo waukali.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

15 Mwaukali ndi mokwiya ndidzalanga mitundu yonse ya anthu imene sidandimvere.”

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

15 Ndidzayilanga mwaukali ndi mokwiya mitundu imene sinandimvere Ine.”

Onani mutuwo Koperani




Mika 5:15
6 Mawu Ofanana  

kubwezera chilango akunja, ndi kulanga mitundu ya anthu;


Chifukwa chake Ambuye ati, Yehova wa makamu wamphamvu wa Israele, Ha! Ndidzatonthoza mtima wanga pochotsa ondivuta, ndi kubwezera chilango adani anga;


ndidzasankhiratu inu kulupanga, ndipo inu nonse mudzagwada ndi kuphedwa; pakuti pamene ndinaitana, inu simunayankhe; pamene ndinanena, simunamve; koma munachita choipa m'maso mwanga, ndi kusankha chimene Ine sindinakondwere nacho.


Ndipo otsala a Yakobo adzakhala mwa amitundu, pakati pa mitundu yambiri ya anthu, ngati mkango mwa nyama zakuthengo, ngati msona wa mkango mwa magulu a nkhosa; umenewo ukapitako, upondereza, numwetula, ndipo palibe wakupulumutsa.


Tamverani tsono chonena Yehova: Nyamuka, tsutsana nao mapiri, ndi zitunda zimve mau ako.


m'lawi lamoto, ndi kubwezera chilango kwa iwo osamdziwa Mulungu, ndi iwo osamvera Uthenga Wabwino wa Ambuye wathu Yesu;


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa