Mika 5:15 - Buku Lopatulika15 Ndipo ndidzabwezera amitundu osamvera chilango mu mkwiyo waukali. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201415 Ndipo ndidzabwezera amitundu osamvera chilango mu mkwiyo waukali. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa15 Mwaukali ndi mokwiya ndidzalanga mitundu yonse ya anthu imene sidandimvere.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero15 Ndidzayilanga mwaukali ndi mokwiya mitundu imene sinandimvere Ine.” Onani mutuwo |