Mika 4:9 - Buku Lopatulika9 Tsono ufuulitsa chifukwa ninji? Palibe mfumu mwa iwe kodi? Watayika kodi mu uphungu wako, kuti zowawa zakugwira ngati mkazi wobala? Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20149 Tsono ufuulitsa chifukwa ninji? Palibe mfumu mwa iwe kodi? Watayika kodi mu uphungu wako, kuti zowawa zakugwira ngati mkazi wobala? Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa9 Kodi ukuliriranji mokuŵa chonchi mzinda iwe? Ukusaukiranji ngati mkazi pa nthaŵi yake yochira? Kodi ndiye kuti ulibe mfumu, kapena phungu wokulangiza? Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero9 Chifukwa chiyani tsopano ukulira mofuwula, kodi ulibe mfumu? Kodi phungu wako wawonongedwa, kotero kuti ululu wako uli ngati wa mayi amene akubereka? Onani mutuwo |