Mika 4:8 - Buku Lopatulika8 Ndipo iwe, nsanja ya nkhosa, chitunda cha mwana wamkazi wa Ziyoni, udzafikira iwe, inde udzafika ulamuliro wakale, ufumu wa mwana wamkazi wa Yerusalemu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20148 Ndipo iwe, nsanja ya nkhosa, chitunda cha mwana wamkazi wa Ziyoni, udzafikira iwe, inde udzafika ulamuliro wakale, ufumu wa mwana wamkazi wa Yerusalemu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa8 “Tsono iwe Ziyoni, nsanja yotetezera nkhosa zanga, phiri la anthu anga, zimene ndidaakulonjeza zidzachitikadi. Ufumu wako wakale uja udzakubwereranso, Anthu a ku Yerusalemu ufumu wao uja udzafikanso.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero8 Kunena za iwe, nsanja ya ziweto zanga, iwe linga la mwana wamkazi wa Ziyoni, ulamuliro wako wakale udzabwezeretsedwa kwa iwe; ufumu udzabwera pa mwana wamkazi wa Yerusalemu.” Onani mutuwo |