Mika 2:7 - Buku Lopatulika7 Kodi adzati, Nyumba ya Yakobo iwe, Mzimu wa Yehova waperewera kodi? Izi ndi ntchito zake kodi? Mau anga samchitira zokoma kodi, iye amene ayenda choongoka? Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20147 Kodi adzati, Nyumba ya Yakobo iwe, Mzimu wa Yehova waperewera kodi? Izi ndi ntchito zake kodi? Mau anga samchitira zokoma kodi, iye amene ayenda choongoka? Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa7 Monga zoterezi nzoyenera kuzinena, inu a banja la Yakobe? Kodi kuleza mtima kwa Chauta kwatheratu? Kodi zimenezi nzimene adachita? Kodi mau ake sadzetsa zabwino kwa munthu woyenda molungama?” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero7 Inu nyumba ya Yakobo, monga zimenezi ndi zoyenera kuzinena: “Kodi Mzimu wa Yehova wakwiya? Kodi Iye amachita zinthu zotere?” “Kodi mawu ake sabweretsa zabwino kwa amene amayenda molungama? Onani mutuwo |
Chifukwa chanji ndinafika osapeza munthu? Ndi kuitana koma panalibe wina woyankha? Kodi dzanja langa lafupika konse, kuti silingathe kuombola? Pena Ine kodi ndilibe mphamvu zakupulumutsa? Taona pa kudzudzula kwanga ndiumitsa nyanja, ndi kusandutsa mitsinje chipululu; nsomba zake zinunkha chifukwa mulibe madzi, ndipo zifa ndi ludzu.